Перейти к содержимому

Utatu ndi Khristu | Ahnsahnghong

World Mission Society Church of God / Global

0:00 / 0:00

Utatu ndi Khristu | Ahnsahnghong

821 просмотр · 3 года назад
World Mission Society Church of God / Global
142 тыс. подписчиков
821 просмотр · 3 года назад
Mpingo wa Mulungu Umakhulupirira mwa Mulungu Yehova, Yesu, ndi Khristu Ahnsahnghong Awo amene amamvetsetsa Utatu angakhulupirire ndi kuzindikira kuti zimene Mulungu Yehova anachita zinachitidwa ndi Yesu, ndipo zimene Yesu anachita zinachitidwa ndi Dzina Latsopano loti Khristu Ahnsahnghong. Athanso kumvetsetsa kuti mu badwo wa Mzimu Woyera, Khristu Ahnsahnghong ayenera kubwera ndi Mulungu Amayi, Mkwatibwi wa Mzimu Woyera ndi kutsogolera anthu ku chipulumutso kudzera mu Paska wa pangano latsopano. Yesaya 43:11 Ine, Inetu ndine Yehova; ndipo palibe Mpulumutsi, koma Ine ndekha. Machitidwe 4:11-12 Iye ndiye . . . Ndipo palibe chipulumutso mwa wina yense, pakuti palibe dzina lina pansi pa thambo la kumwamba, lopatsidwa mwa anthu, limene tiyenera kupulumutsidwa nalo. [Kanema uyu ndi wotsindikizidwa ndi Gulu la Utumiki wa Dziko lapansi la Mpingo wa Mulungu. Malo osalolezedwa kapena kugawa ndi koletsedwa.] 〖World Mission Society Church of God〗https://watv.org 〖 WATV Media Cast 〗 https://watvmedia.org/ny 〖Church of God Introduction〗 https://introwmscog.com