Ndikhulupilira Bible (Official Music Video) — Area 47 Senior Youth Choir
Area 47 Senior Youth Choir
0:00 / 0:00
Ndikhulupilira Bible (Official Music Video) — Area 47 Senior Youth Choir
208 739 просмотров · 6 месяцев назад
Area 47 Senior Youth Choir
5,85 тыс. подписчиков
208 739 просмотров · 6 месяцев назад
Words & Music: Ndudirim Nwachukwu
Accessed from: Tunefulness.scores
Title: Oh yes, I believe
@tunefulness.scores
_________________________________________
Chichewa Lyrics:
1. Ndikhulupilira Bible,
Ndukhulupilira Yesu,
Kuti anafa pamtanda kufera 'ne.
Ndikhulupirira Tate, Mwana ndi Mzimu Oyera,
Ine, ine, ndikhulupira.
Chorus
Kuti anandiferane,
Kuti ndikhale ndi moyo.
Anafa, anafa, anafa kufera ine,
Akufuna ndisiye tchimo, anafa pamtanda paja,
Nagwazidwa Mbuye wanga.
2. Ndikhulupilira Yesu,
Abweradi posachedwa,
Kudzatenga onse kunka nawo mwamba.
Kuti tikhale ndi moyo,
Osatha mudziko ilo,
Ine ine ndikhulupira.