Banja la Kumwamba komanso Nzeru | GUDMWM, Mpingo wa Mulungu
World Mission Society Church of God / Global
0:00 / 0:00
Banja la Kumwamba komanso Nzeru | GUDMWM, Mpingo wa Mulungu
867 просмотров · 2 г. назад
World Mission Society Church of God / Global
144 тыс. подписчиков
867 просмотров · 2 г. назад
Kodi Nzeru Yaikulu Kwambiri Imene Anthu
Ayenera Kukhala Nayo Imene Solomoni
Analemba M’Buku la Mlaliki N’chiyani?
Atasangalala ndi zinthu zonse zimene anthu
a m’dzikoli ankalakalaka, Solomoni pomalizira pake
anafika potsimikiza kuti chilichonse cha
padziko lapansi n’chachabechabe, kungothamangitsa
mphepo, ndiponso kuti anthu ayenera kuopa
Mulungu ndi kumvera mawu Ake kuti alandire madalitso.
N’chifukwa Chiyani Mpingo wa Mulungu
Ukuonekera Padziko Lonse Masiku Ano?
Mulungu amadalitsa amene amasunga malamulo ake,
ndipo amawakweza pamwamba pa mitundu yonse.
Monga momwe Mfumu Hezekiya ndi Yosiya
ya kummwera kwa Yuda adadalitsidwa chifukwa
chomvera mawu a Mulungu, Mpingo wa Mulungu
umatamandidwa ndi kukwezedwa padziko lonse
lapansi chifukwa chogwiritsa ntchito ziphunzitso
za Khristu Ahnsahnghong ndi Amayi akumwamba.
Deuteronomo 28:1-2
Ndipo kudzali, mukadzamvera mau a Yehova
Mulungu wanu mwachangu, ndi kusamalira kuchita
malamulo ake onse amene ndikuuzani lero, kuti
Yehova Mulungu wanu adzakukulitsani koposa
amitundu onse a padziko lapansi;
ndipo madalitso awa onse adzakugwerani, ndi
kukupezani, mukadzamvera mau a Yehova Mulungu wanu. . . .
[Kanema uyu ndi wotsindikizidwa ndi Gulu la Utumiki wa Dziko lapansi la Mpingo wa Mulungu. Malo osalolezedwa kapena kugawa ndi koletsedwa.]
〖World Mission Society Church of God〗https://watv.org
〖 WATV Media Cast 〗 https://watvmedia.org/ny
〖Church of God Introduction〗 https://introwmscog.com